Ezekieli 7:9 OCCL

[9] Ine sindidzakumvera chisoni kapena kukuleka. Ndidzakulanga malingana ndi ntchito zako ndiponso chifukwa cha miyambo yako yonyansa pakati pako. ‘Pamenepo udzadziwa kuti Ine Yehova ndine amene ndimakantha.’

About this translation

Life Bible app icon
Get the Life Bible app Read offline, sync highlights and notes, and study with your library on any device.