2 Mafumu 19:32 OCCL

[32] “Choncho chimene Yehova akunena za mfumu ya ku Asiriya ndi ichi: “ ‘Iye sadzalowa mu mzinda umenewu kapena kuponyamo muvi. Sadzayandikira mzindawu ndi zishango zake kapena kumanga nthumbira ya nkhondo.

About this translation

Life Bible app icon
Get the Life Bible app Read offline, sync highlights and notes, and study with your library on any device.